Marko 6:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anadziitanira khumi ndi awiriwo, nayamba kuwatumiza iwo awiriawiri; nawapatsa mphamvu pa mizimu yonyansa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anadziitanira khumi ndi awiriwo, nayamba kuwatumiza iwo awiriawiri; nawapatsa mphamvu pa mizimu yonyansa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Yesu adaitana ophunzira ake khumi ndi aŵiri aja, naŵatuma aŵiriaŵiri. Adaŵapatsa mphamvu zotulutsira mizimu yoipitsa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Atayitana khumi ndi awiriwo, Iye anawatuma awiriawiri ndipo anawapatsa ulamuliro pa mizimu yoyipa. Onani mutuwo |