Marko 6:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo anazizwa chifukwa cha kusakhulupirira kwao. Ndipo anayendayenda m'midzi yozungulirapo, naphunzitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo anazizwa chifukwa cha kusakhulupirira kwao. Ndipo anayendayenda m'midzi yozungulirapo, naphunzitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo adadabwa poona kuti anthu akumeneko sadamkhulupirire. Pambuyo pake Yesu adapita ku midzi yozungulira, namakaphunzitsa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo Iye anadabwa chifukwa chakusowa chikhulupiriro kwawo. Pamenepo Yesu anayenda mudzi ndi mudzi kuphunzitsa. Onani mutuwo |