Marko 6:52 - Buku Lopatulika52 pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 chifukwa anali asanamvetse bwino za buledi zija. Mitu yao idaali youma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 popeza sanazindikire zimene zinachitika pa malofu a buledi; pakuti mitima yawo inali yowuma. Onani mutuwo |