Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:52 - Buku Lopatulika

52 pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 chifukwa anali asanamvetse bwino za buledi zija. Mitu yao idaali youma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 popeza sanazindikire zimene zinachitika pa malofu a buledi; pakuti mitima yawo inali yowuma.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:52
9 Mawu Ofanana  

Yehova bwanji mwatisocheretsa kusiya njira zanu, ndi kuumitsa mitima yathu tisakuopeni? Bwerani, chifukwa cha atumiki anu, mafuko a cholowa chanu.


Ndipo chitatha icho anaonekera kwa khumi ndi mmodzi iwo okha, alikuseama pachakudya; ndipo anawadzudzula chifukwa cha kusavomereza kwao ndi kuuma mtima, popeza sanavomereze iwo amene adamuona, atauka Iye.


Ndipo m'mene anawaunguza ndi mkwiyo, ndi kumva chisoni chifukwa cha kuuma kwa mitima yao, ananena kwa munthuyo, Tambasula dzanja lako. Ndipo analitambasula; ndipo linachira dzanja lake.


Ndipo ananena nao, Mutero inunso opanda nzeru kodi? Kodi simuzindikira kuti kanthu kalikonse kochokera kunja kukalowa mwa munthu, sikangathe kumdetsa iye;


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Wadetsa maso ao, naumitsa mtima wao; kuti angaone ndi maso, angazindikire ndi mtima, nangatembenuke, ndipo ndingawachiritse.


Ndipo chiyani tsono? Ichi chimene Israele afunafuna sanachipeze; koma osankhidwawo anachipeza, ndipo otsalawo anaumitsidwa mtima;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa