Marko 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo anatulutsa ziwanda zambiri, nadzoza mafuta anthu ambiri akudwala, nawachiritsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo anatulutsa ziwanda zambiri, nadzoza mafuta anthu ambiri akudwala, nawachiritsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ankatulutsa mizimu yoipa yocholuka, ndiponso ankadzoza mafuta anthu odwala ambiri nkumaŵachiritsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Anatulutsa ziwanda zambiri ndi kudzoza mafuta odwala ambiri ndi kuwachiritsa. Onani mutuwo |