Marko 6:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo mfumu Herode anamva izi; pakuti dzina lake lidamveka; ndipo ananena, kuti, Yohane Mbatizi wauka kwa akufa, ndipo chifukwa chake mphamvu izi zichitachita mwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo mfumu Herode anamva izi; pakuti dzina lake lidamveka; ndipo ananena, kuti, Yohane Mbatizi wauka kwa akufa, ndipo chifukwa chake mphamvu izi zichitachita mwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mfumu Herode adaazimva zimenezi, pakuti mbiri ya Yesu inali itamveka ponseponse. Anthu ena ankati, “Yohane Mbatizi uja adauka kwa akufa, nkuwona akuchita zamphamvu zonsezi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mfumu Herode anamva zimenezi, pakuti dzina la Yesu linali litadziwika kwambiri. Ena amati, “Yohane Mʼbatizi waukitsidwa kwa akufa, ndipo nʼchifukwa chake mphamvu zochita zodabwitsa zinkagwira ntchito mwa Iye.” Onani mutuwo |