Marko 6:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anatuluka nalalikira kuti anthu atembenuke mitima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anatuluka nalalikira kuti anthu atembenuke mitima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ophunzira aja adapitadi, namakalalikira anthu kuti atembenuke mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anatuluka kupita kukalalikira kuti anthu atembenuke mtima. Onani mutuwo |