Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Iye anatuluka kumeneko; nafika kudziko la kwao; ndipo ophunzira ake anamtsata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Iye anatuluka kumeneko; nafika kudziko la kwao; ndipo ophunzira ake anamtsata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Yesu adachoka kumeneko, nakafika kumudzi kwao. Ophunzira ake adatsagana naye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yesu anachoka kumeneko napita ku mudzi kwawo, pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo.


nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.


Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu, koma m'dziko la kwao ndimo, ndi pakati pa abale ake, ndi m'nyumba yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa