Marko 5:7 - Buku Lopatulika7 ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mokweza mau adati, “Kodi ndakuputani chiyani, Inu Yesu, Mwana wa Mulungu Wopambanazonse? M'dzina la Mulungu ndikukupemphani, musandizunze.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye anafuwula kwambiri nati, “Mukufuna muchite nane chiyani, Yesu Mwana wa Mulungu Wammwambamwamba? Lumbirani kwa Mulungu kuti simundizunza!” Onani mutuwo |