Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 5:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo pakuona Yesu kutali, anathamanga, namgwadira Iye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo pakuona Yesu kutali, anathamanga, namgwadira Iye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Pamene iye adaona Yesu chakutali, adamthamangira nadzamgwadira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ataona Yesu ali patali, anathamanga nagwa pa mawondo ake pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani




Marko 5:6
7 Mawu Ofanana  

Nenani kwa Mulungu, Ha, ntchito zanu nzoopsa nanga! Chifukwa cha mphamvu yanu yaikulu adani anu adzagonjera Inu.


Okhala m'chipululu adzagwadira pamaso pake; ndi adani ake adzaluma nthaka.


Ndipo masiku onse, usiku ndi usana, anakhala m'manda ndi m'mapiri, nafuula, nadzitematema ndi miyala.


ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze.


Ndi ziwanda zomwe zinatuluka mwa ambiri, ndi kufuula, kuti, Inu ndinu Mwana wa Mulungu. Ndipo Iye anazidzudzula, wosazilola kulankhula, chifukwa zinamdziwa kuti Iye ndiye Khristu.


Ameneyo anatsata Paulo ndi ife, nafuula, kuti, Anthu awa ndi akapolo a Mulungu wa Kumwambamwamba, amene akulalikirani inu njira ya chipulumutso.


Ukhulupirira iwe kuti Mulungu ali mmodzi; uchita bwino; ziwanda zikhulupiriranso, ndipo zinthunthumira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa