Marko 5:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo masiku onse, usiku ndi usana, anakhala m'manda ndi m'mapiri, nafuula, nadzitematema ndi miyala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo masiku onse, usiku ndi usana, anakhala m'manda ndi m'mapiri, nafuula, nadzitematema ndi miyala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Usana ndi usiku ankakhala kumandako ndi m'mapiri, akumangofuula ndi kudzipweteka ndi miyala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Usana ndi usiku ankakhala ku manda ndi kumapiri, akulira ndi kudzicheka ndi miyala. Onani mutuwo |