Marko 5:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo anati kwa iye, Mwana wamkaziwe, chikhulupiriro chako chakupulumutsa; muka mumtendere, nukhale wochira chivutiko chako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo anati kwa iye, Mwana wamkaziwe, chikhulupiriro chako chakupulumutsa; muka mumtendere, nukhale wochira chivutiko chako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yesu adamuuza kuti, “Inu mwana wanga, chikhulupiriro chanu chakuchiritsani. Pitani ndi mtendere. Matenda anu atheretu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Anati kwa iye, “Mwana wamkazi, chikhulupiriro chako chakuchiritsa. Pita mu mtendere ndipo khala womasulidwa ku mavuto ako.” Onani mutuwo |