Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 5:33 - Buku Lopatulika

33 Koma mkaziyo anachita mantha, ndi kunthunthumira, podziwa chimene anamchitira iye, nadza, namgwadira, namuuza choona chonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Koma mkaziyo anachita mantha, ndi kunthunthumira, podziwa chimene anamchitira iye, nadza, namgwadira, namuuza choona chonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Apo mai uja adachita mantha nayamba kunjenjemera, chifukwa anali atazindikira zimene zidaamuwonekerazo. Adadza pafupi, nadzigwetsa pansi pamaso pa Yesu, nkumufotokozera zonse monga momwe zidaachitikira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Kenaka mayi uja pozindikira chimene chinamuchitikira, anabwera ndi kugwa pa mapazi ake, ndipo akunjenjemera ndi mantha, anamuwuza zoona zokhazokha.

Onani mutuwo Koperani




Marko 5:33
10 Mawu Ofanana  

Yehova, Mulungu wanga, ndinafuulira kwa Inu, ndipo munandichiritsa.


Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.


Ndipo iwo anachita mantha aakulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?


Ndipo Iye anaunguzaunguza kumuona iye amene adachita ichi.


Ndipo anati kwa iye, Mwana wamkaziwe, chikhulupiriro chako chakupulumutsa; muka mumtendere, nukhale wochira chivutiko chako.


Ndipo Zekariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.


Koma iye ananthunthumira ndi mau awa, nasinkhasinkha kulonjera uku nkutani.


Ndipo mkaziyo pakuona kuti sanabisike, anadza ndi kunthunthumira, nagwa pamaso pake, nafotokoza pamaso pa anthu onsewo chifukwa chake cha kumkhudza Iye, ndi kuti anachiritsidwa pomwepo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa