Marko 5:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo inampempha Iye, kuti, Titumizeni ife mu nkhumbazo, kuti tilowe mu izo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo inampempha Iye, kuti, Titumizeni ife mu nkhumbazo, kuti tilowe mu izo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono mizimu yoipa ija idapempha Yesu kuti, “Tipirikitsireni ku nkhumbazo, tiloleni tikaloŵe m'menemo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ziwandazo zinapempha Yesu kuti, “Titumizeni pakati pa nkhumbazo; ndipo mutilole tilowe mwa izo.” Onani mutuwo |