Marko 5:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anampempha Iye kwambiri kuti asaitulutsire kunja kwake kwa dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anampempha Iye kwambiri kuti asaitulutsire kunja kwake kwa dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo iye adadandaulira Yesu kwambiri kuti mizimuyo asaitulutsire kunja kwa dera limenelo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo anamupempha Yesu mobwerezabwereza kuti asazitulutse mʼderalo. Onani mutuwo |