Marko 4:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo posiya khamulo anamtenga apite nao, monga momwe anali, mungalawa. Ndipo panali ngalawa zina pamodzi ndi Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo posiya khamulo anamtenga apite nao, monga momwe anali, mungalawa. Ndipo panali ngalawa zina pamodzi ndi Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Tsono iwo adasiya khamu la anthu lija, natenga Yesu m'chombo momwe adaalimo. Padaalinso zombo zina zotsagana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Atasiya gulu la anthu mʼmbuyo, anamutenga Iye, napita naye monga momwe anali mʼbwatolo. Panalinso mabwato ena pamodzi ndi Iye. Onani mutuwo |