Marko 4:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo panauka namondwe wamkulu wa mphepo, ndi mafunde anagavira mungalawa, motero kuti ngalawa inayamba kudzala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo panauka namondwe wamkulu wa mphepo, ndi mafunde anagavira mungalawa, motero kuti ngalawa inayamba kudzala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono padauka namondwe woopsa. Mafunde ankaloŵa m'chombomo, kotero kuti chidaayamba kudzaza ndi madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Mphepo yamkuntho inabuka, ndipo mafunde anawomba bwatolo, kotero kuti linali pafupi kumira. Onani mutuwo |