Marko 4:27 - Buku Lopatulika27 nakagona ndi kuuka, usiku ndi usana, ndipo mbeu zikamera, ndi kukula, iye sadziwa umo zichitira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 nakagona ndi kuuka, usiku ndi usana, ndipo mbeu zikamera, ndi kukula, iye sadziwa umo zichitira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Iyeyo atha kumangogona usiku, m'maŵa nadzuka, nthaŵi yonseyo mbeu adafesa zija zikumera ndi kukula, mwiniwakeyo osadziŵa m'mene zonsezi zikuchitikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira. Onani mutuwo |