Marko 4:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo ananena, Ufumu wa Mulungu uli wotero, monga ngati munthu akataya mbeu panthaka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo ananena, Ufumu wa Mulungu uli wotero, monga ngati munthu akataya mbeu panthaka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Yesu adaŵauzanso kuti, “Za Ufumu wa Mulungu tingazifanizire motere: munthu afesa mbeu m'munda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka. Onani mutuwo |