Marko 4:28 - Buku Lopatulika28 Nthaka ibala zipatso zake yokha; uyamba mmera, zitsata ngala, pamenepo maso okhwima m'ngalamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Nthaka ibala zipatso zake yokha; uyamba mmera, zitsata ngala, pamenepo maso okhwima m'ngalamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Paja nthaka imabereketsa mbeuzo yokhayokha. Umayamba ndi mmera, kenaka ngala, pambuyo pake njere m'ngala muja zimakhwima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Nthaka pa yokha imatulutsa mbewu, umayamba mʼmera, kenaka ngala, kenaka mbewu yokhwima mʼngalayo. Onani mutuwo |