Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 4:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo ananena ndi iwo, Kodi atenga nyali kuti akaivundikire mbiya, kapena akaiike pansi pa kama, osati kuti akaiike pa choikapo chake?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo ananena ndi iwo, Kodi atenga nyali kuti akaivundikire mbiya, kapena akaiike pansi pa kama, osati kuti akaiike pa choikapo chake?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Tsono Yesu adaŵafunsa kuti, “Kodi anthu amatenga nyale nkuivundikira ndi mbiya, kapena kuibisa kunsi kwa bedi? Suja amaiika pa malo oonekera?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Iye anawawuza kuti, “Kodi umatenga nyale ndi kuyiika pansi pa mbiya kapena pansi pa bedi? Mʼmalo mwake, kodi simuyika pa choyikapo chake?

Onani mutuwo Koperani




Marko 4:21
7 Mawu Ofanana  

Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.


Palibe munthu, atayatsa nyali, aiika m'chipinda chapansi, kapena pansi pa mbiya, koma pa choikapo chake, kuti iwo akulowamo aone kuunika.


Ndipo palibe munthu atayatsa nyali, aivundikira ndi chotengera, kapena kuiika pansi pa kama; koma aiika pa choikapo, kuti iwo akulowamo aone kuunikaku.


Koma kwa yense kwapatsidwa maonekedwe a Mzimu kuti apindule nao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa