Marko 4:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo iwo ofesedwa pa nthaka yabwino ndiwo oterewa akumva mau, nawalandira, nabala zipatso zakupindula makumi atatu, ndi makumi asanu ndi limodzi, ndi makumi khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo iwo ofesedwa pa nthaka yabwino ndiwo oterewa akumva mau, nawalandira, nabala zipatso zakupindula makumi atatu, ndi makumi asanu ndi limodzi, ndi makumi khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma mbeu zofesedwa pa nthaka yabwino zija zikutanthauza anthu amene amamva mau a Mulungu, naŵalandira. Anthu otere amabereka zipatso, mwina makumi atatu, mwina makumi asanu ndi limodzi, mwina makumi khumi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ena, ngati mbewu zofesedwa pa nthaka yabwino, amamva mawu, nawalandira, ndi kubereka zipatso zokwanira makumi atatu, makumi asanu ndi limodzi, kapena ngakhale 100 kuwonjezera pa zomwe zinafesedwa.” Onani mutuwo |