Marko 4:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti kulibe kanthu kobisika, koma kuti kaonetsedwe; kapena kulibe kanthu kanakhala kam'tseri, koma kuti kakaululidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti kulibe kanthu kobisika, koma kuti kaonetsedwe; kapena kulibe kanthu kanakhala kam'tseri, koma kuti kakaululidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pajatu chinthu chilichonse chobisika chidzaululuka, ndipo chilichonse chachinsinsi chidzaonekera poyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pakuti chilichonse chobisika chidzayenera kuwululika, ndi chilichonse chachinsinsi chidzayenera kuonekera poyera. Onani mutuwo |