Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 4:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo ananena nao, Simudziwa kodi fanizo ili? Mukazindikira bwanji mafanizo onse?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo ananena nao, Simudziwa kodi fanizo ili? Mukazindikira bwanji mafanizo onse?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pambuyo pake Yesu adaŵafunsa kuti, “Monga simukulimvetsadi fanizo limeneli? Nanga mudzamvetsa bwanji fanizo lina lililonse?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pamenepo Yesu anawawuza kuti, “Kodi simukulimvetsa fanizoli? Kodi nanga mudzazindikira bwanji fanizo lina lililonse?

Onani mutuwo Koperani




Marko 4:13
12 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


Wofesa afesa mau.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa