Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 4:14 - Buku Lopatulika

14 Wofesa afesa mau.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Wofesa afesa mau.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Wofesa mbeu uja ndi amene amafesa mau a Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Wofesa amafesa mawu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 4:14
13 Mawu Ofanana  

Odala muli inu, amene mubzala m'mbali mwa madzi monse, amene muyendetsa mapazi a ng'ombe ndi bulu.


Munthu aliyense wakumva mau a Ufumu, osawadziwitsai, woipayo angodza, nakwatula chofesedwacho mumtima mwake. Uyo ndiye wofesedwa m'mbali mwa njira.


Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


Ndipo Iye anayankha nati, Wofesa mbeu yabwino ndiye Mwana wa Munthu;


Ndipo ambiri anaunjikana, kotero kuti anasowa malo, ngakhale pakhomo pomwe; ndipo analankhula nao mau.


Ndipo ananena nao, Simudziwa kodi fanizo ili? Mukazindikira bwanji mafanizo onse?


Ndipo iwo ndiwo a m'mbali mwa njira mofesedwamo mau; ndipo pamene anamva, pomwepo akudza Satana nachotsa mau ofesedwa mwa iwo.


Mverani: taonani, wofesa anatuluka kukafesa;


monga anazipereka kwa ife iwo amene anakhala mboni ndi atumiki a mau,


Koma fanizoli litere: Mbeuzo ndizo mau a Mulungu.


Pamenepo ndipo iwo akubalalitsidwa anapitapita nalalikira mauwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa