Marko 3:10 - Buku Lopatulika10 pakuti adawachiritsa ambiri; kotero kuti onse akukhala nazo zowawa anakanikiza Iye, kuti akamkhudze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 pakuti adawachiritsa ambiri; kotero kuti onse akukhala nazo zowawa anakanikiza Iye, kuti akamkhudze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pakuti anali atachiritsa anthu ambiri, ndipo onse amene adaali ndi matenda ankakankhana pofuna kuti amkhudze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti anachiritsa ambiri, kotero kuti iwo amene anali ndi matenda amakankhana kutsogolo kuti amukhudze. Onani mutuwo |