Marko 2:6 - Buku Lopatulika6 Koma anakhalapo ena a alembi akuganizira mumtima mwao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma anakhalapo ena a alembi akuganizira mumtima mwao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma pamenepo panalinso aphunzitsi ena a Malamulo a Mose. Iwowo adayamba kudzifunsa mumtima mwao kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo ena mwa aphunzitsi amalamulo anakhala pansi pomwepo, namaganiza mʼmitima mwawo kuti, Onani mutuwo |