Marko 2:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Poona chikhulupiriro chaocho, Yesu adauza munthu wa ziwalo zakufayo kuti, “Mwana wanga, machimo ako akhululukidwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yesu ataona chikhulupiriro chawo, anati kwa wofa ziwaloyo, “Mwana, machimo ako akhululukidwa.” Onani mutuwo |