Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 2:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anadza kwa Iye otenga munthu wodwala manjenje, wonyamulidwa ndi anthu anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anadza kwa Iye otenga munthu wodwala manjenje, wonyamulidwa ndi anthu anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Anthu ena anai adaanyamula munthu wa ziwalo zakufa, kubwera naye kwa Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Amuna anayi anabwera, atanyamula munthu wofa ziwalo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 2:3
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa