Marko 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ambiri anaunjikana, kotero kuti anasowa malo, ngakhale pakhomo pomwe; ndipo analankhula nao mau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ambiri anaunjikana, kotero kuti anasowa malo, ngakhale pakhomo pomwe; ndipo analankhula nao mau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu ochuluka adasonkhana m'nyumbamo, kotero kuti munalibenso malo ngakhale pakhomo pomwe. Iye ankaŵalalikira mau a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho anthu ambiri anasonkhana kotero kuti panalibenso malo, ngakhale ndi pa khomo pomwe, ndipo Iye anawalalikira mawu. Onani mutuwo |