Marko 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo polowanso Iye mu Kapernao atapita masiku ena, kunamveka kuti ali m'nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo polowanso Iye m'Kapernao atapita masiku ena, kunamveka kuti ali m'nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Patapita masiku pang'ono, Yesu adabwereranso ku Kapernao, anthu nkumva kuti ali kunyumba kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Patapita masiku pangʼono, Yesu atalowanso mu Kaperenawo, zinamveka kuti wabwera ali mʼnyumba. Onani mutuwo |