Marko 2:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo ananena nao, Simunawerenge konse chimene anachichita Davide, pamene adasowa, namva njala, iye ndi iwo amene anali pamodzi naye? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo ananena nao, Simunawerenga konse chimene anachichita Davide, pamene adasowa, namva njala, iye ndi iwo amene anali pamodzi naye? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Iye adati, “Bwanji mukuchita ngati simudaŵerenge konse zimene adaachita Davide, pamene iye ndi anzake adaazingwa nayo njala? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iye anayankha kuti, “Kodi simunawerenge zimene Davide anachita pamene iye ndi anzake anali osowa ndi anamva njala? Onani mutuwo |