Marko 2:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Afarisi ananena ndi Iye, Taona, achitiranji chosaloleka kuchitika tsiku la Sabata? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Afarisi ananena ndi Iye, Taona, achitiranji chosaloleka kuchitika tsiku la Sabata? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Apo Afarisi adafunsa Yesu kuti, “Bwanji ophunzira anuŵa akuchita zimene siziloledwa pa tsiku la Sabata?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Afarisi anati kwa Iye, “Taonani, chifukwa chiyani akuchita chosaloledwa ndi lamulo pa Sabata?” Onani mutuwo |