Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 2:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo kunali kuti anapita Iye pakati pa minda tsiku la Sabata; ndipo ophunzira ake poyenda anayamba kubudula ngala za dzinthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo kunali kuti anapita Iye pakati pa minda tsiku la Sabata; ndipo ophunzira ake poyenda anayamba kubudula ngala za dzinthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Pa tsiku lina la Sabata Yesu ankadutsa m'minda ya tirigu. Akuyenda choncho, ophunzira ake adayamba kuthyolako ngala za tirigu nkumadya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Tsiku lina la Sabata, Yesu amadutsa pakati pa minda ya tirigu, ndipo ophunzira ake amayenda naye limodzi, nayamba kubudula ngala za tiriguyo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 2:23
4 Mawu Ofanana  

Ndipo palibe munthu amatsanulira vinyo watsopano m'matumba akale: pena vinyo adzaphulitsa matumba, ndipo aonongeka vinyo, ndi matumba omwe: koma vinyo watsopano amatsanulira m'matumba atsopano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa