Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 16:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo pamene anakweza maso anaona kuti mwala wakunkhunizidwa, pakuti unali waukulu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo pamene anakweza maso anaona kuti mwala wakunkhunizidwa, pakuti unali waukulu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma poyang'anitsitsa adaona kuti chimwalacho achigubuduza kale; tsonotu chinali chachikuludi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Koma atakweza maso awo, anaona kuti mwala umene unali waukulu kwambiri wagubuduzidwa kale.

Onani mutuwo Koperani




Marko 16:4
7 Mawu Ofanana  

nauika m'manda ake atsopano, osemedwa m'mwala, nakunkhunizira mwala waukulu pakhomo pa manda, nachokapo.


Ndipo iwo anamuka, nasunga manda, nasindikizapo chizindikiro pamwalapo, iwo pamodzi ndi alondawo.


Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndani mwalawo, pakhomo la manda?


Ndipo pamene analowa m'manda, anaona mnyamata alikukhala kumbali ya kudzanja lamanja, wovala mwinjiro woyera; ndipo iwo anadabwa.


Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda.


Koma tsiku loyamba la Sabata anadza Maria wa Magadala mamawa, kusanayambe kucha, kumanda, napenya mwala wochotsedwa kumanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa