Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 16:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndani mwalawo, pakhomo la manda?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndani mwalawo, pakhomo la manda?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ankafunsana kuti, “Kodi ndani akatichotsere chimwala cha pakhomo pa manda chija?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 ndipo anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi akatikugudubuzira mwala pa khomo la manda ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 16:3
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa.


Ndipo pamene anakweza maso anaona kuti mwala wakunkhunizidwa, pakuti unali waukulu ndithu.


Koma tsiku loyamba la Sabata anadza Maria wa Magadala mamawa, kusanayambe kucha, kumanda, napenya mwala wochotsedwa kumanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa