Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 16:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 M'mamaŵa ndithu pa tsiku lotsatira Sabatayo, adapita kumanda kuja, dzuŵa litatuluka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mmamawa, tsiku loyamba la Sabata, dzuwa litangotuluka kumene, anali pa ulendo wopita ku manda

Onani mutuwo Koperani




Marko 16:2
6 Mawu Ofanana  

Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango.


Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.


Ndipo litapita Sabata, Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi Salome, anagula zonunkhira, kuti akadze kumdzoza Iye.


Ndipo analikunena mwa okha, Adzatikunkhunizira ndani mwalawo, pakhomo la manda?


Koma tsiku loyamba la sabata, mbandakucha, anadza kumanda atatenga zonunkhira adazikonza.


Koma tsiku loyamba la Sabata anadza Maria wa Magadala mamawa, kusanayambe kucha, kumanda, napenya mwala wochotsedwa kumanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa