Marko 16:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 M'mamaŵa ndithu pa tsiku lotsatira Sabatayo, adapita kumanda kuja, dzuŵa litatuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mmamawa, tsiku loyamba la Sabata, dzuwa litangotuluka kumene, anali pa ulendo wopita ku manda Onani mutuwo |