Marko 16:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ngakhale atamva kuti Yesu ali moyo, ndipo kuti Maria wamuwona, iwo sadakhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Atamva kuti Yesu ali moyo ndikuti amuona, iwo sanakhulupirire. Onani mutuwo |