Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumpanduko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, wamangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumphandumo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Panali munthu wina, dzina lake Barabasi, amene anali m'ndende pamodzi ndi anthu ena chifukwa choukira Boma ndi kupha anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Munthu wotchedwa Baraba anali mʼndende pamodzi ndi anthu owukira amene anapha anthu pa nthawi ya chipolowe.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:7
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pa nthawi yomweyo anali ndi wandende wodziwika, dzina lake Barabasi.


Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha.


Ndipo khamu la anthu anabwera nayamba kupempha kuti achite monga anali kuwachitira nthawi zonse.


Ndipo anawamasulira amene adaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko ndi kupha munthu, amene iwo anampempha; koma anapereka Yesu mwa chifuniro chao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa