Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Pa nthaŵi ya chikondwerero cha Paska, bwanamkubwa ankaŵamasulira mkaidi mmodzi, yemwe Ayudawo ankapempha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Pa nthawi ya Phwando, panali chizolowezi chomasula munthu wamʼndende amene anthu amupempha.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:6
10 Mawu Ofanana  

Mudziwa kuti akapita masiku awiri, Paska afika, ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kupachikidwa pamtanda.


Koma ananena iwo, pa nthawi ya chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu.


Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumpanduko.


koma Petro anaima kukhomo kunja. Chifukwa chake wophunzira winayo amene anadziwika kwa mkulu wa ansembe, anatuluka nalankhula ndi wapakhomo, nalowetsa Petro.


Ndipo pamenepo anampereka Iye kwa iwo kuti ampachike. Pamenepo anatenga Yesu;


Koma zitapita zaka ziwiri Porkio Fesito analowa m'malo a Felikisi; ndipo Felikisi pofuna kukonda Ayuda anamsiya Paulo m'nsinga.


Koma Fesito pofuna kuyesedwa wachisomo ndi Ayuda, anayankha kwa Paulo, nati, Kodi ufuna kukwera kunka ku Yerusalemu, ndi kuweruzidwa ndi ine pomwepo kunena za zinthu izi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa