Marko 15:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pa nthaŵi ya chikondwerero cha Paska, bwanamkubwa ankaŵamasulira mkaidi mmodzi, yemwe Ayudawo ankapempha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pa nthawi ya Phwando, panali chizolowezi chomasula munthu wamʼndende amene anthu amupempha. Onani mutuwo |