Marko 15:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo asilikali anachoka naye nalowa m'bwalo, ndilo Pretorio; nasonkhanitsa gulu lao lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo asilikali anachoka naye nalowa m'bwalo, ndilo Pretorio; nasonkhanitsa gulu lao lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pamenepo asilikali adaloŵetsa Yesu m'bwalo, kunyumba kwa bwanamkubwa, nasonkhanitsa gulu lonse la asilikali anzao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Asilikali anamutenga Yesu ndi kupita naye mʼkati mwa nyumba yaufumu (dera lokhalako asilikali a mfumu) ndipo anasonkhanitsa gulu lonse la asilikali. Onani mutuwo |