Marko 15:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anamveka Iye chibakuwa, naluka korona waminga, namveka pa Iye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anamveka Iye chibakuwa, naluka korona waminga, namveka pa Iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Adamuveka chovala chofiirira, naluka nsangamutu yaminga nkuiika pamutu pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Anamuveka Iye mwinjiro wofiira, kenaka analuka chipewa cha minga ndi kuyika pa mutu pake. Onani mutuwo |