Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:11 - Buku Lopatulika

11 Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Koma akulu a ansembewo adasonkhezera anthu onse aja kuti apemphe kuŵamasulira Barabasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Koma akulu a ansembe anasonkhezera anthu kuti Pilato amasule Baraba mʼmalo mwa Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:11
6 Mawu Ofanana  

Imvani ichi, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israele; tcherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti chiweruzochi chinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde woyalidwa pa Tabori.


Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.


Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru.


Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzachita chiyani ndi Iye amene mumtchula mfumu ya Ayuda?


Pomwepo anafuulanso, nanena, Si uyu, koma Barabasi. Koma Barabasi anali wachifwamba.


Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa