Marko 15:11 - Buku Lopatulika11 Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma akulu a ansembewo adasonkhezera anthu onse aja kuti apemphe kuŵamasulira Barabasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma akulu a ansembe anasonkhezera anthu kuti Pilato amasule Baraba mʼmalo mwa Yesu. Onani mutuwo |