Marko 15:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adaatero chifukwa adaadziŵa kuti Yesuyo akulu a ansembewo angodzampereka chifukwa cha kaduka chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 podziwa kuti akulu a ansembe anamupereka Yesu kwa iye chifukwa cha nsanje. Onani mutuwo |