Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pilato adaŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna kuti ndikumasulireni Mfumu ya Ayudayi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Kodi mukufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?” Pilato anafunsa,

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:9
7 Mawu Ofanana  

Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru.


Ndipo khamu la anthu anabwera nayamba kupempha kuti achite monga anali kuwachitira nthawi zonse.


Koma muli nao makhalidwe, akuti ndimamasulira inu mmodzi pa Paska; kodi mufuna tsono kuti ndimasulire inu mfumu ya Ayuda?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa