Marko 13:6 - Buku Lopatulika6 Ambiri adzafika m'dzina langa, nadzanena, Ine ndine Iye; nadzasocheretsa ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ambiri adzafika m'dzina langa, nadzanena, Ine ndine Iye; nadzasocheretsa ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chifukwa kudzafika anthu ambiri m'dzina langa namadzanena kuti, ‘Mpulumutsi wolonjezedwa uja ndine,’ ndipo adzasokeza anthu ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Anthu ambiri adzabwera mʼdzina langa, nadzati, ‘Ine ndi Iyeyo,’ ndipo adzanamiza anthu ambiri. Onani mutuwo |