Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 13:23 - Buku Lopatulika

23 Koma yang'anirani; onani ndakuuziranitu zinthu zonse, zisanafike.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Koma yang'anirani; onani ndakuuziranitu zinthu zonse, zisanafike.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Koma inu chenjerani. Ine ndiye ndakuuziranitu zonse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Choncho khalani tcheru; ndakuwuzani zonse nthawi isanafike.

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:23
13 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake akanena kwa inu,


Yang'anirani mupewe aneneri onyenga, amene adza kwa inu ndi zovala zankhosa, koma m'kati mwao ali mimbulu yolusa.


pakuti adzauka Akhristu onyenga ndi aneneri onyenga, ndipo adzachita zizindikiro ndi zozizwitsa, kuti akasocheretse, ngati nkutheka, osankhidwa omwe.


Koma m'masikuwo, chitatha chisautso chimenecho, dzuwa lidzadetsedwa, ndi mwezi sudzapatsa kuunika kwake,


Yang'anirani, dikirani, pempherani: pakuti simudziwa nthawi yake.


Ndipo Yesu anayamba kunena nao, Yang'anirani kuti munthu asakusocheretseni.


Koma inu mudziyang'anire inu nokha; pakuti adzakuperekani inu ku bwalo la akulu a milandu; ndipo adzakukwapulani m'masunagoge; ndipo pamaso pa akazembe ndi mafumu mudzaimirira chifukwa cha Ine, kukhale umboni kwa iwo.


Koma mudziyang'anire nokha, kuti kapena mitima yanu ingalemetsedwe ndi madyaidya ndi kuledzera, ndi zosamalira za moyo uno, ndi kuti tsiku ilo lingafikire inu modzidzimutsa ngati msampha;


Ndipo Iye anati, Yang'anirani musasocheretsedwe; pakuti ambiri adzadza m'dzina langa, nadzanena, Ndine amene; ndipo, Nthawi yayandikira; musawatsate pambuyo pao.


Ndipo tsopano ndakuuzani chisanachitike, kuti pamene chitachitika mukakhulupirire.


Inu, tsono, okondedwa, pozizindikiratu izi, chenjerani, kuti potengedwa ndi kulakwa kwa iwo osaweruzika, mungagwe kusiya chikhazikiko chanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa