Marko 13:23 - Buku Lopatulika23 Koma yang'anirani; onani ndakuuziranitu zinthu zonse, zisanafike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma yang'anirani; onani ndakuuziranitu zinthu zonse, zisanafike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma inu chenjerani. Ine ndiye ndakuuziranitu zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Choncho khalani tcheru; ndakuwuzani zonse nthawi isanafike. Onani mutuwo |