Marko 13:24 - Buku Lopatulika24 Koma m'masikuwo, chitatha chisautso chimenecho, dzuwa lidzadetsedwa, ndi mwezi sudzapatsa kuunika kwake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma m'masikuwo, chitatha chisautso chimenecho, dzuwa lidzadetsedwa, ndi mwezi sudzapatsa kuunika kwake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 “Masiku amenewo, mavutowo atatha, dzuŵa lidzada, mwezi udzaleka kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Koma masiku amenewo, masautsowo atatha, “ ‘dzuwa lidzada, ndipo mwezi sudzawala; Onani mutuwo |