Marko 13:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo pamenepo wina akati kwa inu, Onani Khristu ali pano; kapena, Onani, uko; musavomereze; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo pamenepo wina akati kwa inu, Onani Khristu ali pano; kapena, Onani, uko; musavomereze; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Pa nthaŵi imeneyo, wina akadzakuuzani kuti, ‘Ali panotu Khristu uja,’ kapena kuti, ‘Uyo ali apoyo,’ musadzakhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pa nthawi imeneyo, ngati wina adzati kwa inu, ‘Taonani, Khristu ali kuno, kapena, Taonani, uyo ali apoyo!’ musakhulupirire. Onani mutuwo |