Marko 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa: koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, yemweyo adzapulumutsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa: koma iye wakupirira kufikira chimaliziro, yemweyo adzapulumutsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Anthu onse adzadana nanu chifukwa cha Ine. Koma yemwe adzalimbikire mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Anthu onse adzakudani chifukwa cha Ine, koma amene adzalimbika mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke. Onani mutuwo |