Marko 12:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Kodi mwini munda wamphesa uja adzachita chiyani? Ndithu, adzabwera naŵapha alimiwo, munda uja nkuubwereka alimi ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Kodi nanga mwini munda wamphesa adzachita chiyani? Iye adzabwera ndi kupha alimiwo nadzapereka munda wamphesawo kwa ena. Onani mutuwo |